Reload
{"id":67336,"created_at":"2019-04-29 10:53:27","updated_at":"2021-04-20 20:13:30","deleted_at":null,"published_at":"2019-04-29 10:53:27","original_id":null,"artist_id":18543,"title":"Alonda by LUKI","slug":"alonda-by-luki","status":"published","description":null,"album_id":null,"streets":1,"source_type":"s3","source":"file","lyrics":"LYRICS\r\n\r\nSong Title: Alonda\r\n\r\nArtist:LUKI \r\n\r\nProduction: King Duda\r\n\r\n\r\n\r\nVERSE 1\r\n\r\nTilila misozi lero\r\n\r\nKukuwa mwana wapita dzulo \r\n\r\nKa nyenyezi kaja\r\n\r\nsikadzawalanso\r\n\r\nChimwemwe chija\r\n\r\nSitidzachimvanso\r\n\r\n\r\n\r\nUlumali chiphyinjo chodetsa nkhawa \r\n\r\nKhunguli chifukwa cholanda moyo.\r\n\r\n\r\n\r\nHOOK \r\n\r\nIfe ndife ndi alonda\r\n\r\nndife alonda\r\n\r\ntonse ndife alonda X3\r\n\r\nVERSE 2\r\n\r\nMlonda wa mmbale wanga\r\n\r\nAlubino\r\n\r\nAkuyenda ndi mantha\r\n\r\nKuthawitsa moyo\r\n\r\n\r\n\r\nNgat ndiwe neba neba\r\n\r\nMmudzi mwathu ndife amodzi\r\n\r\nTikaima tonse pamodzi nkhanza titha kuzigonjetsa\r\n\r\n\r\n\r\nPoti sa nasankhe kukhala osiyana nafe\r\n\r\nPoti Sanasankhe chonde tisawataye\r\n\r\nIwo sanasankhe moyo tisawalande\r\n\r\nAahh eheh \r\n\r\n\r\n\r\nHOOK \r\n\r\nIfe ndife ndi alonda\r\n\r\nndife alonda\r\n\r\ntonse ndife alonda X3\r\n\r\n\r\n\r\nVERSE 3\r\n\r\nIfe ndife alonda\r\n\r\nTitenge mbali samala mmbale wathu chikondi dzoola\r\n\r\nNgati mafuta nyali tiwale tithandize anzathu kuona \r\n\r\nZoona\r\n\r\nAti ufuna dola\r\n\r\nNkhwilu ya chuma yaletsa kuona zoona\r\n\r\n\r\n\r\nMtima wanga ulila neh\r\n\r\nMoyo wanzawotu zowona ayesa ndi golide\r\n\r\nKoma afuwula bwanji akawandimva awopa mawa apita neh\r\n\r\nMalawi bwanji\r\n\r\nWaleka kuopa chauta ukukhetsa mwazi mwazi\r\n\r\nWathu ufanana \r\n\r\nWasambila mmanja ulendo wokafumbataaa\r\n\r\n\r\n\r\nTembenuka umuyang\u2019ane \r\n\r\nKulichete akukuwabe\r\n\r\nUdindo wathu tisamalane\r\n\r\nFrom Chitipa to nsanje tonse\r\n\r\n\r\n\r\nHOOK \r\n\r\nIfe ndife ndi alonda\r\n\r\nndife alonda\r\n\r\ntonse ndife alonda X3","download_count":267,"play_count":10,"restrict_download":0,"generated_thumbnail":null,"flag_count":0,"download_count_24":1,"download_count_24_at":"2021-04-20","reupload_sent":0,"thumb_path":"https:\/\/s3.eu-central-1.amazonaws.com\/sol-assets\/uploads\/public\/5cc\/6b8\/e98\/thumb_206018_300_300_0_0_crop.jpg","status_reason":null,"status_reason_alt":null,"tags":[]}
Alonda by LUKI

Luki247

Alonda by LUKI

Loading your song...
Downloads: 267

Song Lyrics:

LYRICS Song Title: Alonda Artist:LUKI Production: King Duda VERSE 1 Tilila misozi lero Kukuwa mwana wapita dzulo Ka nyenyezi kaja sikadzawalanso Chimwemwe chija Sitidzachimvanso Ulumali chiphyinjo chodetsa nkhawa Khunguli chifukwa cholanda moyo. HOOK Ife ndife ndi alonda ndife alonda tonse ndife alonda X3 VERSE 2 Mlonda wa mmbale wanga Alubino Akuyenda ndi mantha Kuthawitsa moyo Ngat ndiwe neba neba Mmudzi mwathu ndife amodzi Tikaima tonse pamodzi nkhanza titha kuzigonjetsa Poti sa nasankhe kukhala osiyana nafe Poti Sanasankhe chonde tisawataye Iwo sanasankhe moyo tisawalande Aahh eheh HOOK Ife ndife ndi alonda ndife alonda tonse ndife alonda X3 VERSE 3 Ife ndife alonda Titenge mbali samala mmbale wathu chikondi dzoola Ngati mafuta nyali tiwale tithandize anzathu kuona Zoona Ati ufuna dola Nkhwilu ya chuma yaletsa kuona zoona Mtima wanga ulila neh Moyo wanzawotu zowona ayesa ndi golide Koma afuwula bwanji akawandimva awopa mawa apita neh Malawi bwanji Waleka kuopa chauta ukukhetsa mwazi mwazi Wathu ufanana Wasambila mmanja ulendo wokafumbataaa Tembenuka umuyang’ane Kulichete akukuwabe Udindo wathu tisamalane From Chitipa to nsanje tonse HOOK Ife ndife ndi alonda ndife alonda tonse ndife alonda X3

Subscribe to get the hottest exclusive music and content straight to your inbox!

Register for Slikour On Life
Sign in for Slikour On Life